Konzani Zomasulira
Thandizani kukonza Zomasulira za Google muzilankhulo zimene mumalankhula. Thandizani ku Gulu Lomasulira kuti muthandize anthu padziko lonse kudziwa chinenero chanu.
Lembani mopanda kanthumo kapena sankhani yankho lolondola
Timakusonyezani mawu, kenako inuyo mumamasulira. Kapena mukhoza kungodina ndipo tikusonyezani mawu osiyanasiyana amene tikuganiza kuti ndi kumasulira kwake, ndipo inuyo mutiuza ngati ali olondola kapena osalondola.
Yesetsani kuti mudziwike ndiponso mupeze mabaji
Muli m'gulu la 100 Club, ndi kupitirira: nthawi iliyonse imene mwathandiza, mumachulukitsa mwayi wanu wopeza baji yotsatira.
Chititsani kuti zilankhulo zikhale zamoyo
Gulu Lomasulira ndi gawo lalikulu la ndondomeko yathu yoikira zinenero zatsopano mu Zomasulira za Google. Ngati mumalankhula chinenero chimene tikumasulira, mungatithandize kuti tiike chinenerocho m'gulu la zinenero zina.